1 Mbiri 11:4 - Buku Lopatulika4 Namuka Davide ndi Aisraele onse naye ku Yerusalemu, ndiwo Yebusi; ndipo Ayebusi nzika za m'dziko zinali komweko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Namuka Davide ndi Aisraele onse naye ku Yerusalemu, ndiwo Yebusi; ndipo Ayebusi nzika za m'dziko zinali komweko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pambuyo pake Davide pamodzi ndi Aisraele onse adapita kukathira nkhondo mzinda wa Yerusalemu, ndiye kuti Yebusi, kumene kunkakhala Ayebusi nzika za dzikolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Davide ndi Aisraeli onse anapita ku Yerusalemu (ku Yebusi). Ayebusi amene ankakhala kumeneko Onani mutuwo |