1 Mbiri 11:12 - Buku Lopatulika12 Ndi pambuyo pake Eleazara mwana wa Dodo Mwahohi, ndiye mmodzi wa atatu aja amphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndi pambuyo pake Eleazara mwana wa Dodo Mwahohi, ndiye mmodzi wa atatu aja amphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mnzake wotsatana naye mwa anthu atatu amphamvu aja anali Eleazara, mwana wa Dodo, Mwahohi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Wotsatana naye anali Eliezara mwana wa Dodo Mwahohi, mmodzi mwa ankhondo atatu amphamvu. Onani mutuwo |