1 Mbiri 11:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo Aisraele onse anasonkhana kwa Davide ku Hebroni, ndi kuti, Taonani, ife ndife fupa lanu, ndi mnofu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo Aisraele onse anasonkhana kwa Davide ku Hebroni, ndi kuti, Taonani, ife ndife fupa lanu, ndi mnofu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Aisraele onse adadzasonkhana kwa Davide ku Hebroni. Adamuuza kuti, “Ifetu ndi inuyo tili magazi amodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Aisraeli onse anasonkhana pamaso pa Davide ku Hebroni ndipo anati, “Ife ndife abale anu. Onani mutuwo |