1 Mbiri 10:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo m'mawa mwake anafika Afilisti kuvula za ophedwa, napeza Saulo ndi ana ake adagwa paphiri la Gilibowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo m'mawa mwake anafika Afilisti kuvula za ophedwa, napeza Saulo ndi ana ake adagwa pa phiri la Gilibowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 M'maŵa mwake, Afilisti atabwera kudzafunkha za anthu ophedwawo, adapeza Saulo ataphedwa pamodzi ndi ana ake pa phiri la Gilibowa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mmawa mwake, Afilisti atabwera kudzatenga zinthu za anthu ophedwa, anapeza Sauli ndi ana ake atafa pa phiri la Gilibowa. Onani mutuwo |