Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 10:6 - Buku Lopatulika

6 Momwemo anafa Saulo, ndi ana ake atatu; ndi nyumba yake yonse idafa pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Momwemo anafa Saulo, ndi ana ake atatu; ndi nyumba yake yonse idafa pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Umu ndimo m'mene adafera Saulo, iyeyo ndi ana ake atatu, pamodzi ndi banja lake lonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Motero Sauli ndi ana ake atatu anafa, pamodzi ndi banja lake lonse anafera limodzi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 10:6
8 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene wonyamula zida zake anaona kuti Saulo wafa, anagwera nayenso lupanga lake, nafa.


Ndipo pamene amuna onse a Israele okhala m'chigwamo anaona kuti anathawa, ndi kuti Saulo ndi ana ake adafa, anasiya mizinda yao, nathawa; nadza Afilisti, nakhala m'menemo.


Koma mukaumirirabe kuchita choipa, mudzaonongeka, inu ndi mfumu yanu yomwe.


Chomwecho adamwalira pamodzi Saulo ndi ana ake atatu, ndi wonyamula zida zake, ndi anthu ake onse, tsiku lomwe lija.


Ndipo kunali, pakunena za likasa la Mulungu, iye anagwa chambuyo pa mpando wake pambali pa chipata, ndi khosi lake linathyoka, nafa iye; popeza anali wokalamba ndi wamkulu thupi. Ndipo adaweruza anthu a Israele zaka makumi anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa