1 Mbiri 10:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo pamene wonyamula zida zake anaona kuti Saulo wafa, anagwera nayenso lupanga lake, nafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo pamene wonyamula zida zake anaona kuti Saulo wafa, anagwera nayenso lupanga lake, nafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Wonyamula zida uja ataona kuti Sauloyo wafa, nayenso adadzigwetsa pa lupanga lake, nkufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mnyamata wonyamula zida zake uja ataona kuti Sauli wafa, nayenso anadzigwetsera pa lupanga lake nafa. Onani mutuwo |