1 Mbiri 10:3 - Buku Lopatulika3 Ndi nkhondoyi inamkulira Saulo, ndi amauta anampeza; ndipo anatenga nkhawa chifukwa cha amauta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndi nkhondoyi inamkulira Saulo, ndi amauta anampeza; ndipo anatenga nkhawa chifukwa cha amauta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nkhondo idampanikiza kwambiri Sauloyo, ndipo anthu amauta adampeza namlasa koopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nkhondo inakula kwambiri mozungulira Sauli ndipo pamene anthu amauta anamupeza, anamuvulaza. Onani mutuwo |