1 Mbiri 10:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Afilisti anaumirira kutsata Saulo ndi ana ake, ndi Afilistiwo anapha Yonatani, ndi Abinadabu, ndi Malikisuwa, ana a Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Afilisti anaumirira kutsata Saulo ndi ana ake, ndi Afilistiwo anawapha Yonatani, ndi Abinadabu, ndi Malikisuwa, ana a Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Afilistiwo adapanikiza Saulo ndi ana ake, ndipo adapha Yonatani, Abinadabu ndi Malikisuwa ana a Saulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Afilisti anapanikiza kwambiri Sauli ndi ana ake, ndipo anapha Yonatani, Abinadabu ndi Maliki-Suwa. Onani mutuwo |