Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 10:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo anaika zida zake m'nyumba ya milungu yao, napachika mutu wake m'nyumba ya Dagoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo anaika zida zake m'nyumba ya milungu yao, napachika mutu wake m'nyumba ya Dagoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono adaika zida za Sauloyo m'nyumba ya milungu yao, ndipo adakhomerera mutu wakewo ku nyumba ya Dagoni, mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Iwo anayika zida zake zankhondo mʼnyumba zopembedzera milungu yawo ndipo anapachika mutu wake mʼnyumba ya Dagoni.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 10:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo onse a Yabesi-Giliyadi, atamva zonse Afilisti adachitira Saulo,


Ndipo anamvula natenga mutu wake, ndi zida zake, natumiza ku dziko la Afilisti pozungulirapo, kulalika m'mafano ao ndi mwa anthu.


Ndipo anaika zida zake m'nyumba ya Asitaroti; napachika mtembo wake ku linga la ku Beteseani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa