Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:7 - Buku Lopatulika

7 Ndi ana a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, Kitimu, ndi Rodanimu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndi ana a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, Kitimu, ndi Rodanimu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ana a Yavani naŵa: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:7
12 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, ndi Kitimu, ndi Dodanimu.


Ndi ana a Gomeri: Asikenazi, Difati, ndi Togarima.


Ana a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, Puti, ndi Kanani.


Mafumu a ku Tarisisi ndi ku Zisumbuzo adzabwera nacho chopereka; mafumu a ku Sheba ndi Seba adzadza nazo mphatso.


Katundu wa Tiro. Kuwani, inu ngalawa za Tarisisi; chifukwa wapasudwa, kulibenso nyumba, kulibe polowera; kuchokera kudziko la Kitimu kwavumbulutsidwa kwa iwo.


Ndipo Iye anati, Iwe sudzakondwanso konse, iwe namwali wovutidwa, mwanawamkazi wa Sidoni; uka, oloka kunka ku Kitimu; ngakhale kumeneko iwe sudzapumai.


Ndipo ndidzaika chizindikiro pakati pao, ndipo ndidzatumiza onse amene apulumuka mwa iwo kwa amitundu, kwa Tarisisi, kwa Puti ndi kwa Aludi, okoka uta kwa Tubala ndi Yavani, kuzisumbu zakutali, amene sanamve mbiri yanga, ngakhale kuona ulemerero wanga; ndipo adzabukitsa ulemerero wanga pakati pa amitundu.


Pakuti pitani ku zisumbu za Kitimu nimuone; tumizani ku Kedara nimulingalire bwino; nimuone ngati chinalipo chotere.


Anasema nkhafi zako za thundu wa ku Basani, anapanga mipando yako yamnyanga, woika mu mtengo wanaphini wochokera ku zisumbu za Kitimu.


Thanga lako ndi labafuta wopikapika wa ku Ejipito, likhale ngati mbendera yako; chophimba chako ndicho nsalu yamadzi ndi yofiirira zochokera ku zisumbu za Elisa.


Pakuti zombo za ku Kitimu zidzafika kuyambana naye; chifukwa chake adzatenga nkhawa, nadzabwerera, nadzaipidwa mtima ndi chipangano chopatulika, nadzachita chifuniro chake; adzabweranso, nadzasamalira otaya chipangano chopatulika.


Koma zombo zidzafika kuchokera ku dooko la Kitimu, ndipo adzasautsa Asiriya, nadzasautsa Eberi, koma iyenso adzaonongeka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa