1 Mbiri 1:7 - Buku Lopatulika7 Ndi ana a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, Kitimu, ndi Rodanimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi ana a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, Kitimu, ndi Rodanimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ana a Yavani naŵa: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu. Onani mutuwo |
Ndipo ndidzaika chizindikiro pakati pao, ndipo ndidzatumiza onse amene apulumuka mwa iwo kwa amitundu, kwa Tarisisi, kwa Puti ndi kwa Aludi, okoka uta kwa Tubala ndi Yavani, kuzisumbu zakutali, amene sanamve mbiri yanga, ngakhale kuona ulemerero wanga; ndipo adzabukitsa ulemerero wanga pakati pa amitundu.