Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:51 - Buku Lopatulika

51 Namwalira Hadadi. Ndipo mafumu a Edomu ndiwo mfumu Timna, mfumu Aliva, mfumu Yeteti;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Namwalira Hadadi. Ndipo mafumu a Edomu ndiwo mfumu Timna, mfumu Aliva, mfumu Yeteti;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Hadadi nayenso nkufa. Mafumu a ku Edomu anali aŵa: Timna, Aliva, Yeteti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:51
4 Mawu Ofanana  

Amenewa ndi mafumu a ana aamuna a Esau: ana aamuna a Elifazi woyamba wa Esau: mfumu Temani, mfumu Omara, mfumu Zefo, mfumu Kenazi,


Maina a mafumu obadwa kwa Esau, monga mabanja ao, monga malo ao, monga maina ao ndi awa: mfumu Timna, mfumu Aliva, mfumu Yeteti,


Namwalira Baala-Hanani; ndi Hadadi anakhala mfumu m'malo mwake; ndipo dzina la mzinda wake ndi Pai; ndi dzina la mkazi wake ndiye Mehetabele mwana wamkazi wa Matiredi mwana wamkazi wa Mezahabu.


mfumu Oholibama, mfumu Ela, mfumu Pinoni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa