Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:5 - Buku Lopatulika

5 Ana a Yafeti: Gomeri, ndi Magogi, ndi Madai, ndi Yavani, ndi Tubala, ndi Meseki, ndi Tirasi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ana a Yafeti: Gomeri, ndi Magogi, ndi Madai, ndi Yavani, ndi Tubala, ndi Meseki, ndi Tirasi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ana a Yafeti naŵa: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Meseki ndi Tirasi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:5
8 Mawu Ofanana  

Nowa, Semu, Hamu, ndi Yafeti.


Ndi ana a Gomeri: Asikenazi, Difati, ndi Togarima.


Tsoka ine, kuti ndili mlendo mu Meseki, kuti ndigonera m'mahema a Kedara!


Yavani, Tubala, Meseki, anagulana nawe malonda; ndi anthu amoyo ndi zotengera zamkuwa anagulana nawe malonda.


Gomeri ndi magulu ake onse, nyumba ya Togarima, ku malekezero a kumpoto, ndi magulu ake onse, mitundu yambiri pamodzi ndi iwe.


Ndipo iwe, wobadwa ndi munthu, nenera motsutsana naye Gogi, uziti, Atero Ambuye Yehova, Taona, nditsutsana nawe Gogi, iwe mfumu yaikulu ya Meseki ndi Tubala;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa