Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:41 - Buku Lopatulika

41 Mwana wa Ana: Disoni. Ndi ana a Disoni: Hamurani, ndi Esibani, ndi Itirani, ndi Kerani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Mwana wa Ana: Disoni. Ndi ana a Disoni: Hamurani, ndi Esibani, ndi Itirani, ndi Kerani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni naŵa: Hamurani, Esibani, Itirani, ndi Kerani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:41
4 Mawu Ofanana  

Mafumu obadwa kwa Ahori: mfumu Lotani, mfumu Sobala, mfumu Zibiyoni, mfumu Ana,


Ana a Sobala: Aliyani, ndi Manahati, ndi Ebala, Sefi, ndi Onamu. Ndi ana a Zibiyoni: Aiya ndi Ana.


Ana a Ezere: Bilihani, ndi Zaavani, ndi Yaakani. Ana a Disani: Uzi, ndi Arani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa