Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:16 - Buku Lopatulika

16 ndi Aaravadi, ndi Azemari, ndi Ahamati.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 ndi Aaravadi, ndi Azemari, ndi Ahamati.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Arivadi, Azemari ndi Ahamati.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:16
6 Mawu Ofanana  

ndi Aaravadi, ndi Aazemari, ndi Ahamati; pambuyo pake pamenepo ndipo mabanja a Akanani anafalikira.


Ndipo nthawi yomweyo Solomoni anachita madyerero pamaso pa Yehova Mulungu wathu, ndi Israele yense pamodzi naye, msonkhano waukulu wakuyambira polowera ku Hamati kufikira ku nyanja ya ku Ejipito, masiku asanu ndi awiri, ndi masiku asanu ndi awiri ena, ndiwo masiku khumi mphambu anai.


ndi Ahivi, ndi Aariki, ndi Asini,


Ana a Semu: Elamu, ndi Asiriya, ndi Aripakisadi, ndi Ludi, ndi Aramu, ndi Uzi, ndi Huli, ndi Getere, ndi Meseki.


Okhala mu Sidoni ndi Arivadi ndiwo opalasa ako; anzeru ako, Tiro, okhala mwa iwe, ndiwo oongolera ako.


kuchokera kuphiri la Hori mulinge polowera Hamati; ndipo kutuluka kwake kwa malire kudzakhala ku Zedadi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa