Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:10 - Buku Lopatulika

10 Ndi Kusi anabala Nimirodi; iye anayamba kukhala wamphamvu padziko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndi Kusi anabala Nimirodi; iye anayamba kukhala wamphamvu pa dziko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Kusi adabereka Nimirodi. Iyeyu ndiye adayamba kukhala munthu wamphamvu pa dziko lonse lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:10
4 Mawu Ofanana  

Ndi Ejipito anabala Aludi, ndi Aanamimu, ndi Alehabu, ndi Anafituhimu,


Ndi ana a Kusi: Seba, ndi Havila, ndi Sabita, ndi Raama, ndi Sabiteka. Ndi ana a Raama: Sheba, ndi Dedani.


Ndipo iwo adzatha dziko la Asiriya ndi lupanga, ndi dziko la Nimirodi, ndilo polowera pake; ndipo adzatilanditsa kwa a ku Asiriya pamene alowa m'dziko lathu, pamene aponda m'kati mwa malire athu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa