Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 9:13 - Buku Lopatulika

13 Nati, Mizinda ino mwandipatsayi njotani, mbale wanga? Naitcha dzina lao, Dziko lachikole, kufikira lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Nati, Midzi yino mwandipatsayi njotani, mbale wanga? Naitcha dzina lao, Dziko lachikole, kufikira lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Nchifukwa chake adafunsa kuti, “Kodi iwe mbale wanga, monga ndi imeneyi mizinda imene wandipatsa?” Choncho imatchulidwa kuti dziko la Kabule mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Iye anafunsa kuti, “Mʼbale wanga, kodi iyi nʼkukhala mizinda yondipatsa?” Ndipo iye anayitcha mizindayo Dziko la Kabuli, dzina lomwe amatchedwa mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 9:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Hiramu anatuluka ku Tiro kukaona mizinda adampatsa Solomoniyo, koma siinamkomere.


Atero Yehova, Chifukwa cha zolakwa zitatu za Tiro, kapena zinai, sindidzabweza kulanga kwake; popeza anapereka anthu onse kwa Edomu, osakumbukira pangano lachibale;


nazungulira kotulukira dzuwa ku Betedagoni, nafikira ku Zebuloni ndi ku chigwa cha Ifutahele, kumpoto ku Betemeke, ndi Neiyeli; natulukira ku Kabulu kulamanzere,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa