Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 9:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Hiramu anatuluka ku Tiro kukaona mizinda adampatsa Solomoniyo, koma siinamkomere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Hiramu anatuluka ku Tiro kukaona midzi adampatsa Solomoniyo, koma siinamkomera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Hiramu adabwera kuchokera ku Tiro kuti adzaone mizinda imene Solomoni adampatsa, koma sidamkondweretse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Koma Hiramu atabwera kuchokera ku Turo kudzaona mizinda imene Solomoni anamupatsa, sanasangalatsidwe nayo mizindayo.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 9:12
4 Mawu Ofanana  

popeza Hiramu mfumu ya Tiro adamthandiza Solomoni ndi mitengo yamkungudza ndi yamlombwa ndi golide yemwe, monga momwe iye anafuniramo, chifukwa chake mfumu Solomoni anampatsa Hiramu mizinda makumi awiri m'dziko la Galileya.


Nati, Mizinda ino mwandipatsayi njotani, mbale wanga? Naitcha dzina lao, Dziko lachikole, kufikira lero lino.


Pamenepo Balamu anati kwa mthenga wa Yehova, Ndachimwa, popeza sindinadziwe kuti munaima mondiletsa m'njira; ndipo tsopano, ngati chikuipirani, ndibwerera.


Koma atate wake ndi amai wake ananena naye, Kodi palibe mkazi mwa ana aakazi a abale ako, kapena mwa anthu a mtundu wanga onse, kuti wamuka kutenga mkazi wa Afilisti osadulidwawo? Nati Samisoni kwa atate wake, Nditengereni iye, pakuti andikonda pamaso panga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa