1 Mafumu 9:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo kunali, zitatha zaka makumi awiri m'mene Solomoni adatsiriza nyumba ziwirizo, ndizo nyumba ya Yehova ndi nyumba ya mfumu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo kunali, zitatha zaka makumi awiri m'mene Solomoni adatsiriza nyumba ziwirizo, ndizo nyumba ya Yehova ndi nyumba ya mfumu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ntchito yomanga Nyumba ya Chauta ndi nyumba ya mfumu idamtengera Solomoni zaka makumi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Patatha zaka makumi awiri, ndiye nthawi imene Solomoni anamanga nyumba ziwirizi: Nyumba ya Yehova ndi nyumba yaufumu, Onani mutuwo |