1 Mafumu 9:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo kunali, atatsiriza Solomoni kumanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba ya mfumu, ndi chifuniro chonse cha Solomoni anachikhumbacho, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo kunali, atasiriza Solomoni kumanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba ya mfumu, ndi chifuniro chonse cha Solomoni anachikhumbacho, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Solomoni atamaliza kumanga Nyumba ya Chauta ndi nyumba ya mfumu, ndiponso zonse zimene iye ankafuna kuti amange, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Solomoni atatsiriza kumanga Nyumba ya Yehova ndi nyumba yaufumu, ndi kukwaniritsa kuchita zonse zimene ankafuna, Onani mutuwo |