1 Mafumu 8:9 - Buku Lopatulika9 Munalibe kanthu m'likasamo koma magome awiri aja a mwala Mose anawalongamo pa Horebu, pamene Yehova anapangana ndi ana a Israele, potuluka iwo m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Munalibe kanthu m'likasamo koma magome awiri aja a mwala Mose anawalongamo pa Horebu, pamene Yehova anapangana ndi ana a Israele, potuluka iwo m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 M'Bokosimo munalibe kanthu kena kalikonse, kupatula miyala iŵiri yokha ija imene Mose adaaikamo ku Horebu, kumene Chauta adaachita chipangano ndi Aisraele, iwowo atatuluka ku dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mʼbokosimo munalibe kanthu kena kalikonse kupatula miyala iwiri imene Mose anayikamo ku Horebu, kumene Yehova anachita pangano ndi Aisraeli atatuluka mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |