1 Mafumu 7:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anamanga khonde la mpando wachifumu loweruziramo iye, ndilo khonde la milandu, ndipo linayalidwa ndi mkungudza pansi ndi posanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anamanga khonde la mpando wachifumu loweruziramo iye, ndilo khonde la milandu, ndipo linayalidwa ndi mkungudza pansi ndi posanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adamanganso chigawo china chachikulu chotchedwa Holo ya Mpando Wachifumu, kapena Holo ya Chiweruzo, modzaweruzira milandu. M'kati mwake adaikuta ndi matabwa amkungudza kuyambira pansi mpaka ku siling'i. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anamanga chipinda cha mpando waufumu, Chipinda cha Chilungamo, modzaweruziramo milandu ndipo anayikutira ndi matabwa a mkungudza kuchokera pansi mpaka ku denga. Onani mutuwo |