1 Mafumu 7:47 - Buku Lopatulika47 Ndipo Solomoni anazileka zipangizo zonse osaziyesa, popeza zinachuluka ndithu; kulemera kwake kwa mkuwa wonsewo sikunayeseke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Ndipo Solomoni anazileka zipangizo zonse osaziyesa, popeza zinachuluka ndithu; kulemera kwake kwa mkuwa wonsewo sikunayeseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Koma Solomoni adangozisiya ziŵiya zimenezo osaziyesa pa sikelo, chifukwa zidaalipo zambirimbiri. Motero kulemera kwa mkuŵawo sikudadziŵike. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Solomoni sanayeze ziwiya zonsezi chifukwa zinali zambiri ndipo kulemera kwa mkuwa sikunadziwike. Onani mutuwo |