Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 7:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo panali mazenera m'mizere itatuyo, zenera limodzi lopenyana ndi linzake mizere itatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo panali mazenera m'mizere itatuyo, zenera limodzi lopenyana ndi linzake mizere itatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Panalinso mafuremu a mawindo mizere itatu, windo kupenyana ndi windo linzake. Mawindowo ankapenyana atatuatatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mazenera a nyumbayo anali mmwamba mʼmizere itatu, zenera kuyangʼanana ndi zenera linzake.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 7:4
11 Mawu Ofanana  

Ndipo m'nyumbamo anamanga mazenera a sefa wokhazikika.


Ndipo inayalidwa ndi mkungudza pamwamba pa zipinda makumi anai mphambu zisanu zolongosoledwa pa mapanda, mzere umodzi zipinda khumi mphambu asanu.


Ndipo makomo onse ndi mphuthu zonse zinali zaphwamphwa maonekedwe ake, ndipo zenera limodzi linapenyana ndi linzake mizere itatu.


Ndipo ndidzamanga mazenera ako ndi miyala yofiira, ndi zipata zako ndi bareketi, ndi malire ako onse ndi miyala yokondweretsa.


Ndipo panali mazenera amkati okhazikika pazipinda ndi m'makoma a pakati pao, m'kati mwa chipata pozungulira ponse; momwemonso pamphuthu; ndipo panali mazenera pozungulira ponse m'katimo, ndi pa nsanamirazo panali akanjedza.


Ndi mazenera ake, ndi mphuthu zake, ndi akanjedza ake, anali monga mwa muyeso wa chipata choloza kum'mawa; ndipo anakwerako ndi makwerero asanu ndi awiri, ndi mphuthu zake zinali pakhomo.


Ndimo munali mazenera m'menemo, ndi m'mphuthu zake pozungulirapo, monga mazenera ena aja, m'litali mwake mikono makumi asanu, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri mphambu isanu.


ndi zipinda zake, ndi makoma a pakati pake, ndi mphuthu zake, monga mwa miyeso yomweyi; ndimo munali mazenera m'menemo, ndi m'mphuthu zake pozungulirapo; m'litali mwake mikono makumi asanu, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri mphambu isanu.


ndi zipinda zake, ndi makoma a pakati pake, ndi mphuthu zake, monga mwa miyeso yomweyi; ndimo munali mazenera m'menemo, ndi m'mphuthu zake pozungulirapo, m'litali mwake mikono makumi asanu, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri mphambu isanu.


zipinda zake, makoma a pakati pake, ndi mphuthu zake; ndimo munali mazenera m'menemo pozungulirapo, m'litali mwake mikono makumi asanu, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri mphambu isanu.


Ndipo panali mazenera amkati okhazikika, ndi akanjedza chakuno ndi chauko, kumbali zake za khonde; momwemonso pa zipinda za m'mphepete mwa nyumba, ndi pa matabwa ochindikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa