Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 7:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo panali ngati mapewa anai pansi pangodya zinali za phaka limodzi, mapewawo anali a phaka lomwelo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo panali ngati mapewa anai pansi pangodya zinali za phaka limodzi, mapewawo anali a phaka lomwelo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Phaka lililonse linali ndi zigwiriro zinai, chigwiriro chimodzi pa ngodya iliyonse. Zigwirirozo zidapangidwira kumodzi ndi maphakawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Phaka lililonse linali ndi zogwirira zinayi; chogwirira chimodzi pa ngodya iliyonse, zolumikizidwa ku phakalo.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 7:34
3 Mawu Ofanana  

Ndipo phaka lililonse linali ndi njinga zamkuwa zinai ndi mitanda yamkuwa, ndipo ngodya zake zinai zinali ndi mapewa; pansi pa thawale panali mapewa oyengeka pa mbali pa zophatikizika zonse.


Ndipo mapangidwe a njinga analingana ndi mapangidwe a njinga za galeta, mitanda yake ndi mkombero wake ndi nthiti zake ndi mtima wake zonsezo zinayengedwa.


Ndipo pamwamba pa phaka panali khoma lozunguniza, msinkhu wake nusu ya mkono; ndi pamwamba pa phaka panali mbano zake ndi matsekerezo a phaka lomwelo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa