1 Mafumu 7:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo pamwamba pa nsanamirazo panali ngati akakombo malembedwe ake; motero anaitsiriza ntchito ya nsanamirazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo pamwamba pa nsanamirazo panali ngati akakombo malembedwe ake; motero anaitsiriza ntchito ya nsanamirazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono pamwamba pa nsanamira zija adakongoletsapo ndi zosemasema zooneka ngati maluŵa a kakombo. Motero ntchito ya nsanamirazo idamalizika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mitu ya pamwamba pa nsanamirazo inali yooneka ngati maluwa okongola kwambiri. Motero anamaliza ntchito ya nsanamirazo. Onani mutuwo |