1 Mafumu 7:11 - Buku Lopatulika11 Ndi pamwamba pake panali miyala ya mtengo wapatali, ndiyo miyala yosemasema monga muyeso wake, ndi mitengo yamkungudza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndi pamwamba pake panali miyala ya mtengo wapatali, ndiyo miyala yosemasema monga muyeso wake, ndi mitengo yamkungudza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo pamwamba pake panalinso miyala yabwino kwambiri yosemedwa potsata miyeso yake yofunika, ndiponso pamwamba pa miyalayo panali matabwa amkungudza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pamwamba pake panali pa miyala yabwino kwambiri, yosemedwa potengera miyeso yake. Pamwamba pa miyalayo panali matabwa a mkungudza. Onani mutuwo |