1 Mafumu 6:9 - Buku Lopatulika9 Momwemo anamanga nyumbayo naitsiriza, naika mitanda, naifolera ndi matabwa amikungudza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Momwemo anamanga nyumbayo naitsiriza, naika mitanda, naifolera ndi matabwa amikungudza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Choncho adamanga Nyumbayo mpaka kuimaliza. Ndipo siling'i yake ya Nyumbayo adaipanga ndi mitanda ndi matabwa amkungudza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Choncho anamanga Nyumbayo mpaka kuyimaliza ndipo denga lake linali la mitanda ndi matabwa a mkungudza. Onani mutuwo |