Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 6:8 - Buku Lopatulika

8 Khomo lolowera m'zipinda za pakati linali ku mbali ya ku dzanja lamanja ya nyumba; ndipo anthu amakwerera pa makwerero ozunguniza, kufikira ku zipinda za pakati, ndi kutuluka m'zapakatizo kulowa m'zachitatuzo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Khomo lolowera m'zipinda za pakati linali ku mbali ya ku dzanja lamanja ya nyumba; ndipo anthu amakwerera pa makwerero ozunguniza, kufikira ku zipinda za pakati, ndi kutuluka m'zapakatizo kulowa m'zachitatuzo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Chipata choloŵera ku chipinda chapansi chija chinali chakumwera kwa Nyumbayo. Anthu ankachita kukwera makwerero pochoka ku chipinda chapansi kupita ku chipinda chapakati, chimodzimodzi pochoka ku chipinda chapakati kupita ku chipinda chapamwamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Chipata cholowera ku chipinda chapansi chinali mbali ya kummwera kwa Nyumbayo. Panali makwerero okwerera ku chipinda chapakati ndiponso chipinda cha pamwamba.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 6:8
6 Mawu Ofanana  

Ndipo nyumbayo pomangidwa inamangidwa ndi miyala yokonzeratu asanaitute; ndipo m'nyumbamo simunamveke kulira nyundo, kapena nkhwangwa, kapena chipangizo chachitsulo, pomangidwa iyo.


Momwemo anamanga nyumbayo naitsiriza, naika mitanda, naifolera ndi matabwa amikungudza.


Pamenepo Hezekiya anawauza akonze zipinda m'nyumba ya Yehova; nazikonza.


Pita kunyumba ya Arekabu, nunene nao, nulowetse iwo m'nyumba ya Yehova, m'chipinda china, nuwapatse iwo vinyo amwe.


Pakuti zinasanjikizana pawiri, ndipo zinalibe nsanamira ngati nsanamira za kumabwalo; chifukwa chake zam'mwambazo zinachepa koposa zakunsi ndi pakati kuyambira pansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa