1 Mafumu 6:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo m'nyumbamo anamanga mazenera a sefa wokhazikika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo m'nyumbamo anamanga mazenera a sefa wokhazikika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adaika mawindo amene mafuremu ake anali oloŵa m'kati mwa makoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anapanga mazenera amene maferemu ake anali olowa mʼkati mwa makoma a Nyumbayo. Onani mutuwo |