1 Mafumu 6:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo nyumbayo mfumu Solomoni anaimangira Yehova, m'litali mwake munali mikono makumi asanu ndi limodzi, ndi m'mimba mwake mikono makumi awiri, ndi msinkhu wake mikono makumi atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo nyumbayo mfumu Solomoni anaimangira Yehova, m'litali mwake munali mikono makumi asanu ndi limodzi, ndi m'mimba mwake mikono makumi awiri, ndi msinkhu wake mikono makumi atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nyumba imene mfumu Solomoni adamangira Chauta muutali mwake inali ya mamita 27, muufupi mwake inali ya mamita asanu ndi anai, ndipo msinkhu wake unali wa mamita pafupi 13 ndi theka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Nyumba imene Solomoni anamangira Yehova mulitali mwake inali mamita 27, mulifupi mwake inali mamita asanu ndi anayi, ndipo msinkhu wake unali mamita 13 ndi theka. Onani mutuwo |