Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 5:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Hiramu anatumiza kwa Solomoni, nati, Ndazimva zija munatumiza kwa inezo, ndidzachita chifuniro chanu chonse, kunena za mitengo yamkungudza ndi mitengo yamlombwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Hiramu anatumiza kwa Solomoni, nati, Ndazimva zija munatumiza kwa inezo, ndidzachita chifuniro chanu chonse, kunena za mitengo yamkungudza ndi mitengo yamlombwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ndipo adabweza mau kwa Solomoni akuti, “Ndamva zimene mwandipempha. Ndili wokonzeka kuchita zonse zimene mukufunazo, zoti anthu anga akudulireni mitengo ya mkungudza ndi ya paini.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Tsono Hiramu anabweza mawu awa kwa Solomoni: “Ndalandira uthenga umene mwanditumizira ndipo ine ndidzachita zonse zimene mukufuna pokupatsani mitengo ya mkungudza ndi payini.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 5:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide ndi a nyumba yonse ya Israele anasewera pamaso pa Yehova, ndi zoimbira za mitundumitundu za mlombwa, ndi azeze, ndi zisakasa ndi malingaka, ndi maseche, ndi nsanje.


Ndipo kunachitika, pamene Hiramu anamva mau ake a Solomoni, anakondwera kwakukulu, nati, Alemekezeke Yehova lero amene wampatsa Davide mwana wanzeru akhale mfumu ya anthu aunyinji amenewa.


Akapolo anga adzatsika nayo ku Lebanoni kufika nayo ku nyanja, ndipo ine ndidzaiyandamitsa paphaka kufikira komwe mudzandiuzako, ndi kumeneko ndidzaimasula, ndipo mudzaitenga; nimudzachita chifuniro changa, kumapatsa banja langa zakudya.


Ndipo anatchinga makoma a nyumba m'katimo ndi matabwa amkungudza, kuyambira pansi kufikira posanja, natchinga m'katimo ndi matabwa, nayala pansi m'nyumbamo matabwa amlombwa.


ndi zitseko ziwiri za mitengo yamlombwa pa khomo lina; panali chitseko chopatukana, ndi pa linzake panali chitseko chopatukana.


ndipo ife tidzatema mitengo ku Lebanoni monga mwa kusowa kwanu konse; ndipo tidzabwera nayo kwa inu yoyandamitsa paphaka kufikira ku Yopa; ndipo inu mudzakwera nayo ku Yerusalemu.


M'nyumba yaikulu tsono anatchinga ndi mitengo yamlombwa, imene anaikuta ndi golide wabwino, nalembapo ngati migwalangwa ndi maunyolo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa