1 Mafumu 5:4 - Buku Lopatulika4 Koma tsopano Yehova Mulungu wanga wandipumulitsa ku mbali zonse; palibe wotsutsana nane, kapena choipa chondigwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma tsopano Yehova Mulungu wanga wandipumulitsa ku mbali zonse; palibe wotsutsana nane, kapena choipa chondigwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsopano Chauta Mulungu wanga wandipatsa mtendere mbali zonse za dziko, kotero kuti ndilibe mdani kapena chovuta chilichonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma tsopano Yehova Mulungu wanga wandipatsa mtendere mbali zonse za dziko ndipo ndilibe mdani kapena chovuta chilichonse. Onani mutuwo |