Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 5:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Solomoni anatumiza mau kwa Hiramu, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Solomoni anatumiza mau kwa Hiramu, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndipo Solomoni adabweza mau kwa Hiramu akuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Solomoni anabweza mawu awa kwa Hiramu:

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 5:2
3 Mawu Ofanana  

Mudziwa inu kuti atate wanga Davide sanathe kumangira dzina la Yehova Mulungu wake nyumba, chifukwa cha nkhondo zakumzinga konseko, mpaka atawaika Yehova pansi pa mapazi ake.


Ndipo Solomoni anatumiza kwa Huramu mfumu ya Tiro, ndi kuti, Monga momwe munachitira Davide atate wanga, ndi kumtumizira mikungudza yommangira nyumba yokhalamo, mundichitire ine momwemo.


ndi zakudya za pa gome lake, ndi makhalidwe a anyamata ake, ndi maimiriridwe a atumiki ake, ndi mavalidwe ao, ndi makweredwe ake pokwera iye kunka kunyumba ya Yehova, munalibenso moyo mwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa