Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 5:16 - Buku Lopatulika

16 osawerenga akapitao a Solomoni akuyang'anira ntchito, ndiwo zikwi zitatu mphambu mazana atatu, amenewo analamulira anthu aja akugwira ntchito.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 osawerenga akapitao a Solomoni akuyang'anira ntchito, ndiwo zikwi zitatu mphambu mazana atatu, amenewo analamulira anthu aja akugwira ntchito.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Analinso ndi akapitao 3,300 amene ankayang'anira anthu ogwira ntchito.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 ndi akapitawo 33,000 amene ankayangʼanira ntchitoyi ndiponso anthu ogwira ntchito zina.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 5:16
2 Mawu Ofanana  

Amenewo anali akulu a akapitao oyang'anira ntchito ya Solomoni, mazana asanu mphambu makumi asanu akulamulira anthu ogwira ntchito aja.


Nawerenga Solomoni amuna zikwi khumi mphambu makumi asanu ndi limodzi osenza mirimo, ndi amuna zikwi makumi asanu ndi atatu otema mitengo m'mapiri, ndi zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kuwayang'anira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa