Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 5:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo mfumu Solomoni anasonkhetsa athangata mwa Aisraele onse, ndi athangatawo ndiwo anthu zikwi makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo mfumu Solomoni anasonkhetsa athangata mwa Aisraele onse, ndi athangatawo ndiwo anthu zikwi makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Mfumu Solomoni adayambitsa ntchito yathangata m'dziko lonse la Israele. Ndipo anthu athangatawo analipo 30,000.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mfumu Solomoni inasonkhanitsa anthu ogwira ntchito ya thangata mʼdziko lonse la Israeli ndipo anthu athangatawo analipo 30,000.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 5:13
4 Mawu Ofanana  

ndi Ahisara anayang'anira banja la mfumu, ndi Adoniramu mwana wa Abida anali wamsonkho.


Ndipo chifukwa chake cha msonkho uja anausonkhetsa mfumu Solomoni ndi chimenechi; kuti amange nyumba ya Yehova, ndi nyumba ya iye yekha, ndi Milo, ndi linga la Yerusalemu, ndi Hazori, ndi Megido, ndi Gezere.


Atate wanu analemeretsa goli lathu; inu tsono pepuzaniko ntchito yolemetsa ya atate wanu, ndi goli lake lolemera anatisenzetsali, ndipo tidzakutumikirani.


mwa ana ao otsala m'dziko pambuyo pao, amene ana a Israele sanawathe, mwa iwowa Solomoni anawachititsa thangata mpaka lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa