1 Mafumu 5:10 - Buku Lopatulika10 Tsono Hiramu anapatsa Solomoni mitengo yamkungudza ndi mitengo yamlombwa monga momwe anafuniramo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tsono Hiramu anapatsa Solomoni mitengo yamkungudza ndi mitengo yamlombwa monga momwe anafuniramo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Choncho Hiramu adapereka kwa Solomoni mitengo yonse ya mkungudza ndi ya paini imene ankakhumbayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Motero Hiramu anapereka kwa Solomoni mitengo yonse ya mkungudza ndi payini imene ankayifuna, Onani mutuwo |