Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 4:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo maina ao ndiwo: Benihuri anatengetsa ku mapiri a Efuremu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo maina ao ndiwo: Benihuri anatengetsa ku mapiri a Efuremu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Maina ndi aŵa: Benihuri, ku dziko lamapiri la Efuremu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mayina awo ndi awa: Beni-Huri, wa ku dziko la mapiri la Efereimu;

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 4:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Solomoni anali nao akapitao khumi ndi awiri akuyang'anira Aisraele onse, akufikitsira mfumu ndi banja lake zakudya; aliyense anafikitsa zakudya zofikira mwezi umodzi wa chaka.


monga mwa lamulo la Yehova anampatsa mzinda umene anawapempha, ndiwo Timnati-Sera, ku mapiri a Efuremu; ndipo anamanga mzindawo nakhala m'mwemo.


Eleazaranso mwana wa Aroni anafa; ndipo anamuika paphiri la Finehasi mwana wake, limene adampatsa ku mapiri a Efuremu.


Ndipo ku mapiri a Efuremu kunali munthu dzina lake ndiye Mika.


Ndipo kunali, masiku aja, pamene panalibe mfumu mu Israele, panali munthu Mlevi wogonera kuseri kwa mapiri a Efuremu amene anadzitengera mkazi wamng'ono wa ku Betelehemu ku Yuda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa