Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 4:4 - Buku Lopatulika

4 ndi Benaya mwana wa Yehoyada anali kazembe wa nkhondo, ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 ndi Benaya mwana wa Yehoyada anali kazembe wa nkhondo, ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Benaya mwana wa Yehoyada anali mtsogoleri wankhondo. Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Benaya mwana wa Yehoyada, anali mtsogoleri wa ankhondo; Zadoki ndi Abiatara, anali ansembe;

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 4:4
4 Mawu Ofanana  

ndi Seva anali mlembi; ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe;


Ndipo Benaya mwana wa Yehoyada anayang'anira Akereti ndi Apeleti. Ndipo ana a Davide anali ansembe ake.


Ndipo mfumu inaika Benaya mwana wa Yehoyada m'malo mwake kutsogolera khamu la nkhondo, ndi mfumu inaika Zadoki wansembe m'malo mwa Abiyatara.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa