1 Mafumu 4:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo Solomoni anali nazo zipinda za akavalo a magaleta ake zikwi khumi mphambu ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo Solomoni anali nazo zipinda za akavalo a magaleta ake zikwi khumi mphambu ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndipo Solomoni anali ndi zipinda 40,000 zosungiramo akavalo okoka magareta ake, analinso ndi anthu 12,000 okwera pa akavalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Solomoni anali ndi zipinda 4,000 zodyeramo akavalo okoka magaleta ake ndi anthu 12,000 oyendetsa magaleta. Onani mutuwo |