Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 4:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo akulu a mfumu ndi awa: Azariya mwana wa Zadoki anali wansembe,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo akulu a mfumu ndi awa: Azariya mwana wa Zadoki anali wansembe,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 ndipo nduna zake zikuluzikulu zinali izi: Azariya mwana wa Zadoki anali wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Nduna zake zikuluzikulu zinali izi: Azariya mwana wa Zadoki anali wansembe;

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 4:2
7 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu Solomoni anali mfumu ya Israele yense.


wa Alevi, Hasabiya mwana wa Kemuwele; wa Aroni, Zadoki;


Koma iwe, dzisankhire mwa anthu ako onse, amuna anzeru, akuopa Mulungu, amuna oona, akudana nalo phindu la chinyengo; nuwaikire iwo oterewa, akulu a pa zikwi, akulu a pa mazana, akulu a pa makumi asanu, akulu a pa makumi;


Ndipotu Mulungu anaika ena mu Mpingo, poyamba atumwi, achiwiri aneneri, achitatu aphunzitsi, pamenepo zozizwa, pomwepo mphatso za machiritso, mathandizo, maweruziro, malilime a mitundumitundu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa