Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 4:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo mfumu Solomoni anali mfumu ya Israele yense.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo mfumu Solomoni anali mfumu ya Israele yense.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mfumu Solomoni ankalamulira dziko lonse la Israele,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndipo Mfumu Solomoni inakhala mfumu ya Aisraeli onse.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 4:1
14 Mawu Ofanana  

Ndipo Yowabu anali woyang'anira khamu lonse la Israele; ndi Benaya, mwana wa Yehoyada, anayang'anira Akereti ndi Apeleti;


Ku Hebroni anachita ufumu pa Yuda zaka zisanu ndi ziwiri kudza miyezi isanu ndi umodzi; ndi ku Yerusalemu anachita ufumu pa Aisraele onse ndi Ayuda omwe zaka makumi atatu mphambu zitatu.


Ndipo Davide anakhala mfumu ya Aisraele onse, Davide naweruza ndi chilungamo milandu ya anthu onse.


komatu sindidzachotsa ufumu wonsewo; fuko limodzi ndidzapatsa mwana wako, chifukwa cha Davide mtumiki wanga, ndi chifukwa cha Yerusalemu amene ndinamsankha.


Ndipo mfumu Rehobowamu anafunsira kwa mandoda, amene anaimirira pamaso pa Solomoni atate wake, akali moyo iyeyo, nati, Inu mundipangire bwanji kuti ndiyankhe anthu awa?


Ndipo Aisraele onse anamva maweruzidwe ake idaweruza mfumu, naopa mfumu; pokhala anaona kuti nzeru ya Mulungu inali mwa iye yakuweruza.


Ndipo akulu a mfumu ndi awa: Azariya mwana wa Zadoki anali wansembe,


Onsewa, ndiwo anthu a nkhondo akusunga malongosoledwe a nkhondo, anadza ku Hebroni ndi mtima wangwiro kudzamlonga Davide mfumu ya Aisraele onse; ndi onse otsala a Israele omwe anali a mtima umodzi kumlonga Davide ufumu.


Momwemo Solomoni anadza ku Yerusalemu kuchokera ku msanje uli ku Gibiyoni, ku khomo la chihema chokomanako; ndipo anachita ufumu pa Israele.


Ndipo Solomoni anakhala mfumu ya Israele yense mu Yerusalemu zaka makumi anai.


Nanga Solomoni mfumu ya Israele sanachimwe nazo zinthu izi? Chinkana mwa amitundu ambiri panalibe mfumu ngati iye, ndi Mulungu wake anamkonda, ndi Mulungu wake anamlonga mfumu ya Aisraele onse; koma ngakhale iye, akazi achilendo anamchimwitsa.


Ine Mlaliki ndinali mfumu ya Israele mu Yerusalemu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa