1 Mafumu 3:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo kapolo wanu ndili pakati pa anthu anu amene Inu munawasankha, anthu ambirimbiri osawerengeka, kapena kulembeka mu unyinji wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo kapolo wanu ndili pakati pa anthu anu amene Inu munawasankha, anthu ambirimbiri osawerengeka, kapena kulembeka m'unyinji wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono ine mtumiki wanu ndikukhala pakati pa anthu amene mudaŵasankha, mtundu waukulu, anthu ake ochuluka, oti nkosatheka kuŵaŵerenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mtumiki wanu ali pakati pa anthu amene munawasankha, mtundu waukulu, anthu ochuluka kwambiri osatheka kuwawerenga. Onani mutuwo |