1 Mafumu 3:2 - Buku Lopatulika2 Koma anthu anaphera nsembe pamisanje, popeza panalibe nyumba yomangira dzina la Yehova kufikira masiku omwewo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma anthu anaphera nsembe pamisanje, popeza panalibe nyumba yomangira dzina la Yehova kufikira masiku omwewo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu nsembe ankatsirirabe ku akachisi osiyanasiyana, chifukwa choti nthaŵi imeneyo anali asanammangire nyumba Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma anthu ankaperekabe nsembe ku malo achipembedzo osiyanasiyana chifukwa chakuti mpaka pa nthawi imeneyo Dzina la Yehova anali asanalimangire nyumba. Onani mutuwo |