1 Mafumu 22:9 - Buku Lopatulika9 Tsono mfumu ya Israele anaitana mdindo, nati, Kamtenge msanga Mikaya mwana wa Imila. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Tsono mfumu ya Israele anaitana mdindo, nati, Kamtenge msanga Mikaya mwana wa Imila. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Apo Ahabu adaitana imodzi mwa nduna zake nkuiwuza kuti, “Takaitanani Mikaya, mwana wa Imila, abwere kuno msanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Choncho mfumu ya Israeli inayitana mmodzi mwa atumiki ake ndipo inati, “Kayitane Mikaya mwana wa Imula msangamsanga.” Onani mutuwo |