1 Mafumu 22:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yehosafati ananena ndi mfumu ya Israele, Funsira ku mau a Yehova lero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yehosafati ananena ndi mfumu ya Israele, Funsira ku mau a Yehova lero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Yehosafati adauza Ahabu kuti, “Poyamba upemphe nzeru kwa Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma Yehosafati anawuzanso mfumu ya ku Israeli kuti, “Poyamba mupemphe nzeru kwa Yehova.” Onani mutuwo |