1 Mafumu 22:41 - Buku Lopatulika41 Koma Yehosafati mwana wa Asa anayamba kukhala mfumu ya Yuda chaka chachinai cha Ahabu mfumu ya Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Koma Yehosafati mwana wa Asa anayamba kukhala mfumu ya Yuda chaka chachinai cha Ahabu mfumu ya Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Yehosafati, mwana wa Asa, adayamba kulamulira ku Yuda pa chaka chachinai cha ufumu wa Ahabu, mfumu ya ku Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Yehosafati, mwana wa Asa anakhala mfumu ya ku Yuda chaka chachinayi cha Ahabu mfumu ya ku Israeli. Onani mutuwo |