1 Mafumu 22:4 - Buku Lopatulika4 Tsono anati kwa Yehosafati, Kodi udzapita nane kunkhondo ku Ramoti Giliyadi? Ndipo Yehosafati anati kwa mfumu ya Israele, M'mene ukhalira iwe ndi momwe ndikhalira ndine; anthu anga monga anthu ako, akavalo anga monga akavalo ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tsono anati kwa Yehosafati, Kodi udzapita nane kunkhondo ku Ramoti Giliyadi? Ndipo Yehosafati anati kwa mfumu ya Israele, M'mene ukhalira iwe ndi momwe ndikhalira ndine; anthu anga monga anthu ako, akavalo anga monga akavalo ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndipo adafunsa Yehosafati kuti, “Kodi udzapita nane limodzi ku nkhondo ku Ramoti-Giliyadi?” Yehosafati adauza mfumu ya ku Israeleyo kuti, “Ine ndili nanu limodzi, anthu anga nganu, akavalo anga nganunso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono iye anafunsa Yehosafati kuti, “Kodi udzapita nane ku nkhondo ku Ramoti Giliyadi?” Yehosafati anayankha mfumu ya ku Israeli kuti, “Ine ndili monga inu, anthu anga monga anthu anu, akavalo anga monga akavalo anu.” Onani mutuwo |