1 Mafumu 22:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mfumu ya Israele ananena ndi anyamata ake, nati, Kodi simudziwa kuti Ramoti Giliyadi ngwathu, ndipo tangokhala chete, osaulanditsa m'dzanja la mfumu ya Aramu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo mfumu ya Israele ananena ndi anyamata ake, nati, Kodi simudziwa kuti Ramoti Giliyadi ngwathu, ndipo tangokhala chete, osaulanditsa m'dzanja la mfumu ya Aramu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Ahabu adafunsa aphungu ake kuti, “Ramoti-Giliyadi ndi mzinda wathu, nanga chifukwa chiyani ife tikukhala chete, osaulanda kwa mfumu ya ku Siriya?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mfumu ya ku Israeli nʼkuti itawuza atumiki ake kuti, “Kodi inu simukudziwa kuti Ramoti Giliyadi ndi dera lathu ndipo ife palibe chimene tikuchita kuti tilitenge deralo mʼmanja mwa mfumu ya Aramu?” Onani mutuwo |