1 Mafumu 22:2 - Buku Lopatulika2 Koma kunachitika chaka chachitatu, kuti Yehosafati mfumu ya Yuda anatsikira kwa mfumu ya Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma kunachitika chaka chachitatu, kuti Yehosafati mfumu ya Yuda anatsikira kwa mfumu ya Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pa chaka chachitatu Yehosafati mfumu ya ku Yuda adakacheza kwa Ahabu, mfumu ya ku Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma pa chaka chachitatu, Yehosafati mfumu ya ku Yuda anapita kukacheza ndi mfumu ya ku Israeli. Onani mutuwo |