1 Mafumu 22:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Aaramu ndi Aisraele anakhala chete zaka zitatu, osathirana nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Aaramu ndi Aisraele anakhala chete zaka zitatu, osathirana nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Padapita zaka zitatu popanda nkhondo pakati pa Siriya ndi Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kwa zaka zitatu panalibe nkhondo pakati pa Aramu ndi Israeli. Onani mutuwo |