Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mafumu 22:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Aaramu ndi Aisraele anakhala chete zaka zitatu, osathirana nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Aaramu ndi Aisraele anakhala chete zaka zitatu, osathirana nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Padapita zaka zitatu popanda nkhondo pakati pa Siriya ndi Israele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Kwa zaka zitatu panalibe nkhondo pakati pa Aramu ndi Israeli.

Onani mutuwo Koperani




1 Mafumu 22:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Benihadadi anati kwa iye, Ndidzabweza mizinda ija atate wanga analanda kwa atate wanu; ndipo mudzikonzere mabwalo a malonda mu Damasiko, monga umo atate wanga anadzikonzera mu Samariya. Ndi ine, ati Ahabu, ndikulola umuke ndi pangano ili. Tsono anapangana naye, namlola amuke.


Waona umo wadzichepetsera Ahabu pamaso panga? Popeza adzichepetsa pamaso panga, sindidzafikitsa choipa chimenechi akali moyo iye; koma m'masiku a mwana wake ndidzachifikitsa pa nyumba yake.


Koma kunachitika chaka chachitatu, kuti Yehosafati mfumu ya Yuda anatsikira kwa mfumu ya Israele.


Ndipo mfumu ya Aramu inalinkuchita nkhondo ndi Israele, nipangana ndi anyamata ake, kuti, Misasa yanga idzakhala pakutipakuti.


Yehosafati tsono anali nacho chuma ndi ulemu zomchulukira, nachita chibale ndi Ahabu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa